Levitiko 27:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo akapatulira Yehova munda woti adaugula, wosati wogawako ku munda wakewake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo akapatulira Yehova munda woti adaugula, wosati wogawako ku munda wakewake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Munthu akapereka kwa Chauta munda umene waugula, umene suli chigawo cha choloŵa chake, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 “ ‘Ngati munthu apereka kwa Yehova munda umene anagula, umene si malo a makolo ake, Onani mutuwo |