Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 27:20 - Buku Lopatulika

20 Koma akapanda kuombola mundawo, kapena atagulitsa mundawo kwa munthu wina, suomboledwanso;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Koma akapanda kuombola mundawo, kapena atagulitsa mundawo kwa munthu wina, suomboledwanso;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Koma ngati safuna kuti aombole kapena ngati waugulitsa kwa munthu wina, mundawo sudzaombolekanso.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Koma ngati sawuwombola mundawo, kapena ngati waugulitsa kwa munthu wina, mundawo sudzawomboledwanso.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 27:20
3 Mawu Ofanana  

Ndipo wakupatula mundayo akauomboladi, aonjezeko limodzi la magawo asanu la ndalama za kuyesa kwako, ndipo uzikhalitsa wake.


koma potuluka m'chaka choliza lipenga, mundawo ukhale wopatulikira Yehova, ngati munda woperekedwa chiperekere kwa Mulungu; ukhale wakewake wa wansembe.


Chaka choliza lipenga mundawo ubwerere kwa iye amene adaugulitsa, kwa iye amene dzikoli ndi lakelake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa