Levitiko 27:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo wakupatula mundayo akauomboladi, aonjezeko limodzi la magawo asanu la ndalama za kuyesa kwako, ndipo uzikhalitsa wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo wakupatula mundayo akauomboladi, aonjezeko limodzi la magawo asanu la ndalama za kuyesa kwako, ndipo uzikhalitsa wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Munthu amene adapereka munda, akafuna kuti auwombole, pa mtengo wa mundawo aonjezepo chimodzi mwa zigawo zisanu za mtengowo, ndipo udzakhala wake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ngati munthu amene wapereka munda afuna kuwuwombola, ayenera kuwonjezera pa mtengo wake wa mundawo, limodzi mwa magawo asanu a mtengowo. Ndipo mundawo udzakhalanso wake. Onani mutuwo |