Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 27:17 - Buku Lopatulika

17 Akapatula munda wake kuyambira chaka choliza lipenga, mundawo ukhale monga momwe unauyesera.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Akapatula munda wake kuyambira chaka choliza lipenga, mundawo ukhale monga momwe unauyesera.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Akapereka munda wake kuyambira pa chaka chokondwerera zaka 50, mtengo wake ukhale wathunthu monga momwe iwe udaikira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Ngati munthu apereka munda wake kuyambira chaka chokondwerera zaka makumi asanu, mtengo wake ukhale umene unakhazikitsidwa.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 27:17
7 Mawu Ofanana  

Ndipo muchipatule chaka cha makumi asanu, ndi kulalikira kwa onse okhala m'dzikomo kuti akhale aufulu; muchiyese chaka choliza lipenga; ndipo mubwerere munthu aliyense ku zakezake, ndipo mubwerere yense ku banja lake.


Muchiyese chaka cha makumi asanucho choliza lipenga, musamabzala, kapena kucheka zophuka zokha m'mwemo; kapena kucheka mphesa zake za mipesa yosadzombola.


Chaka choliza lipenga ichi mubwerere nonse ku zakezake.


Pamenepo uzitumizira lipenga lomveka m'mwezi wachisanu ndi chiwiri, tsiku lakhumi la mweziwo; tsiku la chitetezero mutumizire lipenga lifikire m'dziko lanu lonse.


Munthu akapatula nyumba yake ikhale yopatulika kwa Yehova, wansembe aziiyesa mtengo wake, ingakhale yokoma kapena yoipa; monga wansembeyo aiyesa, ikhale momwemo.


Munthu akapatulirako Yehova munda wakewake, uziuyesa monga mwa mbeu zake zikakhala; homeri wa barele uuyese wa masekeli makumi asanu a siliva.


Akaupatula munda wake chitapita chaka choliza lipenga, wansembe azimwerengera ndalama monga mwa zaka zotsalira kufikira chaka choliza lipenga, nazichepsako pa kuyesa kwako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa