Levitiko 27:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo akaiombola ndithu, pamenepo aonjezepo limodzi la magawo asanu la mtengo wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo akaiombola ndithu, pamenepo aonjezepo limodzi la magawo asanu la mtengo wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Koma akafuna kuti aiwombole, aonjezepo pa mtengo wake wa nyamayo chimodzi mwa zigawo zisanu za mtengo wakewo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ngati mwini wakeyo akufuna kuwombola nyamayo, awonjezere pa mtengo wake wa nyamayo chimodzi mwa zigawo zisanu zamtengowo. Onani mutuwo |