Levitiko 27:12 - Buku Lopatulika12 ndipo wansembeyo aiyese mtengo wake, ingakhale yokoma kapena yoipa; monga uiyesa wansembewe, momwemo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 ndipo wansembeyo aiyese mtengo wake, ingakhale yokoma kapena yoipa; monga uiyesa wansembewe, momwemo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ndipo wansembe atchule mtengo wake poona ngati njabwino kapena ai. Monga momwe iwe wansembe utchulire, mtengo udzakhala momwemo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 ndipo wansembeyo atchule mtengo wake poona ngati ndi yabwino kapena ndi yoyipa. Mtengo umene wansembe atchule ndiwo udzakhale mtengo wake. Onani mutuwo |