Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 27:10 - Buku Lopatulika

10 Asaisinthe, yokoma m'malo mwa yoipa, kapena yoipa m'malo mwa yokoma; ndipo akasinthadi nyama m'malo mwa inzake, pamenepo iyo ndi yosinthikayo zikhale zopatulika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Asaisinthe, yokoma m'malo mwa yoipa, kapena yoipa m'malo mwa yokoma; ndipo akasinthadi nyama m'malo mwa inzake, pamenepo iyo ndi yosinthikayo zikhale zopatulika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Munthu asapereke ina m'malo mwake kapena kuisinthitsa ndi ina, asapereke yabwino m'malo mwa yoipa, kapena yoipa m'malo mwa yabwino. Ndipo akasinthitsa nyama ina ndi inzake, nyamayo pamodzi ndi inzake waisinthitsayo zikhala zopatulika.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Munthu asasinthanitse ndi ina kapena kupereka ina yabwino mʼmalo mwa yoyipa, kapena yoyipa mʼmalo mwa yabwino. Ngati asinthitsa nyama ina mʼmalo mwa ina, nyamayo pamodzi ndi inzake wasinthitsayo zikhala zopatulika.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 27:10
5 Mawu Ofanana  

Ndipo asagulitseko, kapena kulisintha, kapena kupitiriza zipatso zoyamba za dziko; pakuti lili lopatulika la Yehova.


Ndipo chikakhala cha nyama yodetsa, imene sabwera nayo ikhale chopereka cha Yehova, aike nyamayi pamaso pa wansembe;


Ndipo chikakhala cha nyama imene anthu amabwera nayo ikhale chopereka cha Yehova, zonse zotere munthu akazipereka kwa Yehova zikhale zopatulika.


munthu wa mitima iwiri akhala wosinkhasinkha panjira zake zonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa