Levitiko 26:38 - Buku Lopatulika38 Ndipo mudzatayika mwa amitundu, ndi dziko la adani anu lidzakudyani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201438 Ndipo mudzatayika mwa amitundu, ndi dziko la adani anu lidzakudyani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa38 Mudzatha, kuchita kuti psiti, pakati pa mitundu ya anthu, ndipo dziko la adani anu lidzakudyani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero38 Mudzatheratu pakati pa mitundu ya anthu. Dziko la adani anu lidzakudyani. Onani mutuwo |