Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 26:38 - Buku Lopatulika

38 Ndipo mudzatayika mwa amitundu, ndi dziko la adani anu lidzakudyani.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

38 Ndipo mudzatayika mwa amitundu, ndi dziko la adani anu lidzakudyani.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

38 Mudzatha, kuchita kuti psiti, pakati pa mitundu ya anthu, ndipo dziko la adani anu lidzakudyani.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

38 Mudzatheratu pakati pa mitundu ya anthu. Dziko la adani anu lidzakudyani.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 26:38
10 Mawu Ofanana  

Ndipo padzakhala tsiku limenelo, lipenga lalikulu lidzaombedwa; ndipo adzafika omwe akadatayika m'dziko la Asiriya, ndi opirikitsidwa a m'dziko la Ejipito; ndipo adzapembedza Yehova m'phiri lopatulika la pa Yerusalemu.


koma kumene anamtengera iye ndende, kumeneko adzafa, ndipo sadzaonanso dziko ili.


Tsopano mudziwetu kuti mudzafa ndi lupanga, ndi njala ndi mliri, komwe mufuna kukakhalako.


Ndipo otsala mwa inu adzazunzika m'moyo ndi mphulupulu zao m'maiko a adani anu; ndiponso ndi mphulupulu za makolo ao adzazunzika m'moyo.


chifukwa chake mudzatumikira adani anu amene Yehova adzakutumizirani, ndi njala, ndi ludzu, ndi usiwa, ndi kusowa zinthu zonse; ndipo adzaika goli lachitsulo pakhosi panu, kufikira atakuonongani.


Ndipo Yehova adzakubwezerani ku Ejipito ndi ngalawa, panjira imene ndinati kwa inu, kuti, Simudzaionanso; ndipo kumeneko mudzadzigulitsa kwa adani anu mukhale akapolo ndi adzakazi; koma palibe wogula inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa