Levitiko 26:26 - Buku Lopatulika26 Pamene ndithyola mchirikizo wanu wa mkate, akazi khumi adzaphika mkate wanu mu mchembo umodzi, nadzabweza mkate wanu ndi kuuyesa; ndipo mudzadya, koma osakhuta. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Pamene ndithyola mchirikizo wanu wa mkate, akazi khumi adzaphika mkate wanu mu mchembo umodzi, nadzabweza mkate wanu ndi kuuyesa; ndipo mudzadya, koma osakhuta. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Ndidzachepetsa buledi wanu wa tsiku ndi tsiku mpaka akazi khumi adzapanga buledi mu uvuni umodzi. Ndipo adzakugaŵirani bulediyo pang'onopang'ono. Choncho mudzadya, koma osakhuta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Ndikadzachepetsa buledi wanu, akazi khumi adzaphika buledi wawo mu uvuni umodzi, ndipo adzakugawirani bulediyo pangʼonopangʼono. Choncho mudzadya koma wosakhuta. Onani mutuwo |