Levitiko 26:22 - Buku Lopatulika22 Popeza ndidzatumiza chilombo chakuthengo pakati pa inu, ndipo chidzalanda ana anu, ndi kuononga zoweta zanu ndipo chidzachepetsa inu kuti mukhale pang'ono; ndi njira zanu zidzakhala zakufa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Popeza ndidzatumiza chilombo cha kuthengo pakati pa inu, ndipo chidzalanda ana anu, ndi kuononga zoweta zanu nichidzachepetsa inu kuti mukhale pang'ono; ndi njira zanu zidzakhala zakufa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Ndidzabweretsanso zilombo zolusa pakati panu, zimene zidzakudyerani ana anu, ndi kukuwonongerani ng'ombe zanu. Zilombozo zidzachepetsa chiŵerengero chanu, kotero kuti m'njira zanu simuzidzapita anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Ndidzabweretsa zirombo zolusa pakati panu, ndipo zidzakulandani ana anu ndi kuwononga ngʼombe zanu. Choncho zidzachepetsa chiwerengero chanu kotero kuti mʼnjira mwanu simudzapita anthu. Onani mutuwo |