Levitiko 26:20 - Buku Lopatulika20 ndipo mudzachita nayo mphamvu yanu chabe; ndi nthaka yanu siidzapereka zipatso zake, ndi mitengo ya m'dziko siidzabala zobala zake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 ndipo mudzachita nayo mphamvu yanu chabe; ndi nthaka yanu siidzapereka zipatso zake, ndi mitengo ya m'dziko siidzabala zobala zake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Nyonga zanu zidzapita pachabe, poti nthaka yanu sidzabala kanthu, ndipo mitengo yake sidzabala zipatso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Mphamvu zanu zidzapita pachabe chifukwa nthaka yanu sidzabala kanthu, ngakhale mitengo yake sidzabala zipatso zake. Onani mutuwo |