Levitiko 26:18 - Buku Lopatulika18 Ndipo mukapanda kundimvera, zingakhale izi, ndidzaonjeza kukulangani kasanu ndi kawiri chifukwa cha zochimwa zanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Ndipo mukapanda kundimvera, zingakhale izi, ndidzaonjeza kukulangani kasanu ndi kawiri chifukwa cha zochimwa zanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Mukapanda kundimvera mutaona zonsezi, ndidzakulanganinso mochulukitsa kasanunkaŵiri chifukwa cha machimo anu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 “ ‘Ngati simudzandimvera mutaona zonsezi, ndidzakulanganinso mochulukitsa kasanu ndi kawiri chifukwa cha kuchimwa kwanu. Onani mutuwo |