Levitiko 26:11 - Buku Lopatulika11 Ndidzamanga Kachisi wanga pakati pa inu, ndipo moyo wanga sudzanyansidwa nanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndidzamanga Kachisi wanga pakati pa inu, ndipo moyo wanga sudzanyansidwa nanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Ndidzakhala pakati panu ndipo sindidzaipidwa nanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Ndidzakhala pakati panu, ndipo sindidzayipidwa nanu. Onani mutuwo |
Koma mukayesa dziko la cholowa chanu nchodetsa, olokani kulowa m'dziko la cholowa cha Yehova m'mene chihema cha Yehova chikhalamo, nimukhale nacho cholowa pakati pa ife; koma musapikisana ndi Yehova kapena kupikisana nafe, ndi kudzimangira nokha guwa la nsembe, pamodzi ndi guwa la nsembe la Yehova Mulungu wathu.