Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 25:3 - Buku Lopatulika

3 Zaka zisanu ndi chimodzi ubzale m'munda mwako, ndi zaka zisanu ndi chimodzi udzombole mpesa zako, ndi kucheka zipatso zake;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Zaka zisanu ndi chimodzi ubzale m'munda mwako, ndi zaka zisanu ndi chimodzi udzombole mphesa zako, ndi kucheka zipatso zake;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Pa zaka zisanu ndi chimodzi muzikalima minda yanu, ndipo muzikathenera mitengo yanu yamphesa ndi kuthyola zipatso zake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Pa zaka zisanu ndi chimodzi muzikalima minda yanu, ndipo kwa zaka zisanu ndi chimodzi muzikasadza mitengo yanu ya mpesa ndi kuthyola zipatso zake.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 25:3
3 Mawu Ofanana  

Ndipo uzibzala m'munda mwako zaka zisanu ndi chimodzi, ndi kututa zipatso zako;


koma chaka chachisanu ndi chiwiri uuleke, ugone; kuti aumphawi a anthu a mtundu wako adyemo, ndipo zotsalira nyama zakuthengo zizidye; momwemo uzichita ndi munda wako wampesa, ndi munda wako wa azitona.


Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mutakalowa m'dziko limene ndikupatsani, dzikoli lizisungira Yehova Sabata.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa