Levitiko 24:7 - Buku Lopatulika7 Nuike lubani loona ku mzere uliwonse, kuti likhale kumkate ngati chokumbutsa, nsembe yamoto ya Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Nuike lubani loona ku mzere uliwonse, kuti likhale kumkate ngati chokumbutsa, nsembe yamoto ya Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Pa mzere uliwonse muikepo lubani wokoma, kuti pamodzi ndi bulediyo akhale chikumbutso cha nsembe yopsereza yopereka kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pa mzere uliwonse muyikepo lubani wafungo lokoma kuti pamodzi ndi bulediyo akhale wachikumbutso cha nsembe yopsereza yopereka kwa Yehova. Onani mutuwo |