Levitiko 24:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo uzitenga ufa wosalala, ndi kuphika timitanda khumi ndi tiwiri; awiri a magawo khumi a efa afikane kamtanda kamodzi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo uzitenga ufa wosalala, ndi kuphika timitanda khumi ndi tiwiri; awiri a magawo khumi a efa afikane kamtanda kamodzi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 “Mutenge ufa wosalala, ndipo muphike makeke khumi ndi aŵiri. Keke iliyonse ikhale ya ufa wokwanira makilogaramu aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 “Mutenge ufa wosalala ndipo muphike makeke khumi ndi awiri ndipo keke iliyonse ikhale ya ufa wa makilogalamu awiri. Onani mutuwo |