Levitiko 24:18 - Buku Lopatulika18 Munthu akakantha nyama kuti ife, ambwezere ina; moyo kulipa moyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Munthu akakantha nyama kuti ife, ambwezere ina; moyo kulipa moyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Munthu wopha choŵeta cha mnzake amlipire china, moyo ulipe moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Aliyense wopha chiweto cha mnzake ayenera kulipira china. Moyo kulipa moyo. Onani mutuwo |