Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 24:18 - Buku Lopatulika

18 Munthu akakantha nyama kuti ife, ambwezere ina; moyo kulipa moyo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Munthu akakantha nyama kuti ife, ambwezere ina; moyo kulipa moyo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Munthu wopha choŵeta cha mnzake amlipire china, moyo ulipe moyo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Aliyense wopha chiweto cha mnzake ayenera kulipira china. Moyo kulipa moyo.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 24:18
5 Mawu Ofanana  

Munthu akafukula dzenje, kapena akakumba dzenje, osalivundikira, ndipo ikagwamo ng'ombe kapena bulu,


Munthu akachititsa mnansi wake chilema, monga umo anachitira momwemo amchitire iye;


Iye wakukantha nyama kuti ife, ambwezere ina; iye wakupha munthu, amuphe.


pamenepo padzali kuti popeza anachimwa, napalamula, azibweza zofunkha zimene analanda mwachifwamba, kapena chinthuchi adachiona ndi kusautsa mnzake, kapena choikiza anamuikiza, kapena chinthu chotayika anachipeza;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa