Levitiko 24:11 - Buku Lopatulika11 ndipo mwana wamwamuna wa mkazi Wachiisraele anachitira Dzina mwano, natemberera; ndipo anadza naye kwa Mose. Dzina la mai wake ndiye Selomiti, mwana wa Dibiri, wa fuko la Dani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 ndipo mwana wamwamuna wa mkazi Wachiisraele anachitira Dzina mwano, natemberera; ndipo anadza naye kwa Mose. Dzina la mai wake ndiye Selomiti, mwana wa Dibiri, wa fuko la Dani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Munthu uja adanyoza dzina la Chauta ndi kulitemberera. Tsono adabwera naye kwa Mose. Dzina la mai wake linali Selomiti, mwana wa Dibiri, wa fuko la Dani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Munthu uja ananyoza dzina la Yehova ndi kulitemberera. Choncho anabwera naye kwa Mose. Dzina la amayi ake linali Selomiti, mwana wa Dibiri, wa fuko la Dani. Onani mutuwo |