Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 23:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Chauta adauzanso Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Yehova anawuza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 23:9
3 Mawu Ofanana  

ndi chikondwerero cha Masika, zipatso zoyamba za ntchito zako, zimene udazibzala m'munda; ndi chikondwerero cha Kututa, pakutha chaka, pamene ututa ntchito zako za m'munda.


Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Mutakalowa m'dziko limene ndikupatsani, ndi kucheka dzinthu zake, pamenepo muzidza nao mtolo wa zipatso zoyamba za masika anu kwa wansembe;


Koma mubwere nayo kwa Yehova nsembe yamoto masiku asanu ndi awiri; pa tsiku lachisanu ndi chiwiri pakhale msonkhano wopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa