Levitiko 23:8 - Buku Lopatulika8 Koma mubwere nayo kwa Yehova nsembe yamoto masiku asanu ndi awiri; pa tsiku lachisanu ndi chiwiri pakhale msonkhano wopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Koma mubwere nayo kwa Yehova nsembe yamoto masiku asanu ndi awiri; pa tsiku lachisanu ndi chiwiri pakhale msonkhano wopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Koma mupereke nsembe yopsereza kwa Chauta pa masiku asanu ndi aŵiri. Tsiku lachisanu ndi chiŵiri ndi tsiku la msonkhano wopatulika, musagwire ntchito zotopetsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Pa masiku asanu ndi awiri muzipereka nsembe yopsereza kwa Yehova. Ndipo tsiku lachisanu ndi chiwiri muzikhala ndi msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito yolemetsa.’ ” Onani mutuwo |