Levitiko 23:5 - Buku Lopatulika5 Mwezi woyamba, tsiku lakhumi ndi chinai la mweziwo, madzulo, pali Paska wa Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mwezi woyamba, tsiku lakhumi ndi chinai la mweziwo, madzulo, pali Paska wa Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 pa mwezi woyamba, tsiku la 14 la mweziwo, madzulo ake, ndi tsiku la Paska ya Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Chikondwerero cha Paska chiziyamba madzulo a tsiku la 14 la mwezi woyamba. Onani mutuwo |