Levitiko 22:8 - Buku Lopatulika8 Asamadya zakufa zokha, kapena zojiwa, kudzidetsa nazo; Ine ndine Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Asamadya zakufa zokha, kapena zojiwa, kudzidetsa nazo; Ine ndine Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Asadye chinthu chofa chokha kapena chojiwa ndi chilombo, ndi kumadziipitsa nazo zimenezo. Ine ndine Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Wansembe sayenera kudya chinthu chofa chokha kapena chojiwa ndi chirombo kuopa kuti angadzidetse ndi chakudyacho. Ine ndine Yehova. Onani mutuwo |