Levitiko 22:7 - Buku Lopatulika7 Koma litalowa dzuwa, adzakhala woyera, ndi pambuyo pake adyeko zoyerazo, popeza ndizo chakudya chake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Koma litalowa dzuwa, adzakhala woyera, ndi pambuyo pake adyeko zoyerazo, popeza ndizo chakudya chake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Adzakhala woyeretsedwa dzuŵa litaloŵa, ndipo pambuyo pake adzatha kudyako zinthu zopatulikazo, poti zimenezo ndi chakudya chake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Munthuyo adzakhala woyeretsedwa pamene dzuwa lalowa, ndipo angathe kudya chopereka chopatulikacho popeza ndi chakudya chake. Onani mutuwo |