Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 22:26 - Buku Lopatulika

26 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Chauta adauza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Yehova anawuza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 22:26
2 Mawu Ofanana  

Ndipo musamazilandira izi ku dzanja la mlendo ndi kubwera nazo zikhale chakudya cha Mulungu wanu; popeza zili nako kuvunda kwao; zili ndi chilema; sizidzalandirikira inu.


Zikamabadwa ng'ombe kapena nkhosa, kapena mbuzi, zikhale ndi make masiku asanu ndi awiri; kuyambira tsiku lachisanu ndi chitatu ndi m'tsogolo mwake, idzalandirika ngati chopereka nsembe yamoto ya Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa