Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 22:24 - Buku Lopatulika

24 Nyama yofula, kapena chophwanya kapena chosansantha, kapena chotudzula, kapena chodula, musamabwera nazo kwa Yehova; inde musamachita ichi m'dziko mwanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Nyama yofula, kapena chopwanya kapena chosansantha, kapena chotudzula, kapena chodula, musamabwera nazo kwa Yehova; inde musamachita ichi m'dziko mwanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 Nyama iliyonse imene mavalo ake ali onyuka kapena otswanyika, kapena ong'ambika kapena oduka, musaipereke ngati nsembe kwa Chauta m'dziko mwanu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 Nyama iliyonse imene mavalo ake ndi onyuka kapena ophwanyika, ongʼambika kapena oduka, musamayipereke kwa Yehova mʼdziko lanu.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 22:24
4 Mawu Ofanana  

kapena wowerama, kapena wamfupi msinkhu, kapena wopunduka diso, kapena munthu wamphere, kapena wachipere, kapena wopunduka kumoto.


Musamabwera nayo yokhala ndi chilema; popeza siidzalandirikira inu.


Ng'ombe kapena nkhosa yokula kapena yochepa chiwalo, ikhale nsembe yaufulu; koma pa chowinda siidzalandirika.


Munthu wofulika kapena woduka chiwalo chaumuna, asalowe m'msonkhano wa Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa