Levitiko 22:22 - Buku Lopatulika22 Musamabwera nazo kwa Yehova yakhungu, kapena yoduka mwendo, kapena yopunduka, kapena yafundo, kapena yausemwe, kapena ya usemwe waukulu, musamazipereka kwa Yehova nsembe zamoto paguwa la nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Musamabwera nazo kwa Yehova yakhungu, kapena yoduka mwendo, kapena yopunduka, kapena yafundo, kapena yausemwe, kapena ya usemwe waukulu, musamazipereka kwa Yehova nsembe zamoto pa guwa la nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Musapereka kwa Chauta nyama zakhungu kapena zopunduka, kapena zoduka chiwalo, kapena zotulutsa mafinya m'thupi, kapena za nthenda zonyerenyesa, kapena zamphere. Nyama zotere asazipereke kwa Chauta, zisakhale nsembe zopsereza pa guwa la Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Musapereke kwa Yehova nyama zakhungu, zovulala kapena zolumala, kapena nyama zimene zikutulutsa mafinya mʼthupi mwake, kapena zimene zili ndi nthenda yonyerenyetsa, kapena zimene zili ndi mphere. Nyama zotere musaziyike pa guwa kuti zikhale nsembe yopsereza kwa Yehova. Onani mutuwo |