Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 22:12 - Buku Lopatulika

12 Ndipo mwana wamkazi wa wansembe akakwatibwa ndi mlendo, asadyeko nsembe yokweza ya zinthu zopatulika.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Ndipo mwana wamkazi wa wansembe akakwatibwa ndi mlendo, asadyeko nsembe yokweza ya zinthu zopatulika.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Mwana wamkazi wa wansembe akakwatiwa ndi wapadera, asadyeko zopereka zopatulikazo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Mwana wamkazi wa wansembe amene wakwatiwa ndi munthu amene si wansembe, asadyeko nsembe zopatulikazo.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 22:12
4 Mawu Ofanana  

Ndani anapangira mzimu wa Yehova, kapena kukhala phungu lake, ndi kumphunzitsa Iye?


ndi chifukwa cha mlongo wake weniweni, akakhala namwali wosakhala naye mwamuna, nkuloleka adzidetse chifukwa cha iwowa.


Koma wansembe atakagula munthu ndi ndalama zake, iyeyu adyeko; ndi iwo amene anabadwa m'nyumba yake, adyeko mkate wake.


Koma mwana wamkazi wa wansembe akakhala wamasiye kapena wochotsedwa, ndipo alibe mwana, nabwerera kunyumba ya atate wake, monga muja anali mwana, adyeko mkate wa atate wake; koma mlendo asamadyako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa