Levitiko 21:9 - Buku Lopatulika9 Akadziipsa mwana wamkazi wa wansembe ndi kuchita chigololo, alikuipsa atate wake, amtenthe ndi moto. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Akadziipsa mwana wamkazi wa wansembe ndi kuchita chigololo, alikuipsa atate wake, amtenthe ndi moto. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Ndipo mwana wamkazi wa wansembe aliyense akadziipitsa pokhala wachiwerewere, amaipitsa bambo wake. Mwanayo ayenera kumtentha pa moto. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “ ‘Ngati mwana wamkazi wa wansembe adziyipitsa pochita zachiwerewere, ndiye kuti iye akuchititsa manyazi abambo ake; mwanayo atenthedwe pa moto. Onani mutuwo |