Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 21:4 - Buku Lopatulika

4 Akakhala mwini banja pakati pa anthu a mtundu wake, asadzidetse, ndi kudziipsa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Akakhala mwini banja pakati pa anthu a mtundu wake, asadzidetse, ndi kudziipsa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Wansembe asadziipitse pa imfa ya munthu amene wakwatira naye ku banja limodzi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Koma wansembe asadzidetse chifukwa cha anthu amene ali nawo pa ubale obwera chifukwa cha ukwati.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 21:4
3 Mawu Ofanana  

ndi chifukwa cha mlongo wake weniweni, akakhala namwali wosakhala naye mwamuna, nkuloleka adzidetse chifukwa cha iwowa.


Asamete tsitsi la pamutu pao, kapena kuchecherera ndevu zao, kapena kudzicheka matupi ao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa