Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 21:3 - Buku Lopatulika

3 ndi chifukwa cha mlongo wake weniweni, akakhala namwali wosakhala naye mwamuna, nkuloleka adzidetse chifukwa cha iwowa.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 ndi chifukwa cha mlongo wake weniweni, akakhala namwali wosakhala naye mwamuna, nkuloleka adzidetse chifukwa cha iwowa.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 kapena mlongo wake wosakwatiwa amene amakhala pafupi naye, poti chikhalire alibe mwamuna.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 kapena mlongo wake wosakwatiwa amene amadalira iye chifukwa sanakwatiwe. Iye akhoza kudzidetsa pokhudza thupi lakufa la mchemwali wake wosakwatiwa yekha.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 21:3
3 Mawu Ofanana  

koma chifukwa cha abale ake enieni ndiwo, mai wake, ndi atate wake, ndi mwana wake wamwamuna, ndi mwana wake wamkazi, ndi mbale wake;


Akakhala mwini banja pakati pa anthu a mtundu wake, asadzidetse, ndi kudziipsa.


Ndipo mwana wamkazi wa wansembe akakwatibwa ndi mlendo, asadyeko nsembe yokweza ya zinthu zopatulika.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa