Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 21:2 - Buku Lopatulika

2 koma chifukwa cha abale ake enieni ndiwo, mai wake, ndi atate wake, ndi mwana wake wamwamuna, ndi mwana wake wamkazi, ndi mbale wake;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

2 koma chifukwa cha abale ake enieni ndiwo, mai wake, ndi atate wake, ndi mwana wake wamwamuna, ndi mwana wake wamkazi, ndi mbale wake;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

2 Koma angathe kukhudza mai wake, bambo wake, mwana wake wamwamuna, mwana wake wamkazi,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

2 Koma akhoza kukhudza thupi lakufa la amayi ake, abambo ake, mwana wake wamwamuna, mwana wake wamkazi, mchimwene wake,

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 21:2
4 Mawu Ofanana  

Asasendere mmodzi wa inu kwa mbale wake kumvula; Ine ndine Yehova.


Asafike kuli mtembo; asadzidetse chifukwa cha atate wake, kapena mai wake.


ndi chifukwa cha mlongo wake weniweni, akakhala namwali wosakhala naye mwamuna, nkuloleka adzidetse chifukwa cha iwowa.


Koma sitifuna, abale, kuti mukhale osadziwa za iwo akugona; kuti mungalire monganso otsalawo, amene alibe chiyembekezo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa