Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 21:13 - Buku Lopatulika

13 Ndipo adzitengere mkazi akali namwali.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Ndipo adzitengere mkazi akali namwali.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Ndipo akwatire mnamwali wosadziŵa mwamuna,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 “ ‘Iye akwatire namwali wosadziwa mwamuna.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 21:13
6 Mawu Ofanana  

Kungakhale kutenga amasiye kapena osudzulidwa akhale akazi ao, asachite; koma atenge anamwali a mbeu ya nyumba ya Israele, kapena wamasiye ndiye wamasiye wa wansembe.


Asatuluke m'malo opatulika, kapena kuipsa malo opatulika a Mulungu wake; popeza korona wa mafuta odzoza wa Mulungu wake ali pa iye; Ine ndine Yehova.


Mkazi wamasiye, kapena womleka, kapena woipsidwa, wachigololo, oterewa asawatenge; koma azitenga namwali wa anthu a mtundu wake akhale mkazi wake.


Asadzitengere mkazi wachigololo, kapena woipsidwa; asatenge mkazi woti adamchotsa mwamuna wake; popeza apatulikira Mulungu wake.


Pakuti ndichita nsanje pa inu ndi nsanje ya Mulungu; pakuti ndinakupalitsani ubwenzi mwamuna mmodzi, kuti ndikalangize inu ngati namwali woyera mtima kwa Khristu.


Iwo ndiwo amene sadetsedwa pamodzi ndi akazi; pakuti ali anamwali. Iwo ndiwo amene atsata Mwanawankhosa kulikonse amukako. Iwowa anagulidwa mwa anthu, zipatso zoyamba kwa Mulungu ndi kwa Mwanawankhosa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa