Levitiko 20:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo musunge malemba anga ndi kuwachita; Ine ndine Yehova wakupatula inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo musunge malemba anga ndi kuwachita; Ine ndine Yehova wakupatula inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Muzimvera malamulo anga ndi kuŵatsata. Ine ndine Chauta amene ndikukuyeretsani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Ndipo sungani malangizo anga ndi kuwatsata. Ine ndine Yehova amene ndimakuyeretsani. Onani mutuwo |