Levitiko 20:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo ngati anthu a m'dzikomo akambisa munthuyo pang'ono ponse, pamene apereka a mbeu zake kwa Moleki, kuti asamuphe; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo ngati anthu a m'dzikomo akambisa munthuyo pang'ono ponse, pamene apereka a mbeu zake kwa Moleki, kuti asamuphe; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Anthu am'dzikomo akachita ngati sakumuwona munthuyo, pamene akupereka mmodzi mwa ana ake kwa Moleki, namleka osamupha, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Ngati anthu a mʼderalo achita ngati sakumuona munthuyo pamene akupereka mwana wake kwa Moleki ndi kusamupha, Onani mutuwo |