Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 20:15 - Buku Lopatulika

15 Mwamuna akagona ndi nyama amuphe ndithu; muiphenso nyamayi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Mwamuna akagona ndi nyama amuphe ndithu; muiphenso nyamayi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Mwamuna akagona ndi nyama, ayenera kuphedwa, ndipo nyamayo muiphenso.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 “ ‘Ngati mwamuna agonana ndi nyama, iye ayenera kuphedwa, ndipo muyeneranso kupha nyamayo.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 20:15
4 Mawu Ofanana  

Aliyense agona ndi choweta aphedwe ndithu.


Ndipo usamagonana ndi nyama iliyonse, kudetsedwa nayo; kapena mkazi asamaima panyama, kugonana nayo; chisokonezo choopsa ichi.


Mkazi akasendera kwa nyama iliyonse kugonana nayo, umuphe mkaziyo, ndi nyama yomwe; muwaphe ndithu; mwazi wao ukhale pamutu pao.


Wotembereredwa iye wakugona ndi nyama iliyonse. Ndi anthu onse anene, Amen.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa