Levitiko 19:8 - Buku Lopatulika8 koma aliyense akudyako adzasenza mphulupulu yake, popeza waipsa chopatulidwa cha Yehova; ndi munthuyu amsadze, kumchotsa kwa anthu a mtundu wake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 koma aliyense akudyako adzasenza mphulupulu yake, popeza waipsa chopatulidwa cha Yehova; ndi munthuyu amsadze, kumchotsa kwa anthu a mtundu wake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Munthu aliyense amene aidye, adzasenza tchimo lake chifukwa chakuti waipitsa chinthu choyera cha Chauta. Munthu ameneyo achotsedwe pakati pa anthu anzake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Munthu aliyense amene adya chakudyacho adzasenza machimo ake chifukwa wayipitsa chinthu chimene ndi choyera kwa Yehova. Munthu ameneyo achotsedwe pakati pa anthu anzake. Onani mutuwo |