Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 19:7 - Buku Lopatulika

7 Akakadya konse tsiku lachitatu kali chonyansa, kosavomerezeka:

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Akakadya konse tsiku lachitatu kali chonyansa, kosavomerezeka:

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Mukaidya pa tsiku lachitatu, kuteroko nkuchita chinthu chonyansa, ndipo nsembeyo sidzalandiridwa.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Ngati mudya choperekacho tsiku lachitatu, ndiye kuti mwachita chonyansa ndipo chakudyacho sichidzalandiridwa.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 19:7
9 Mawu Ofanana  

Musadze nazonso, nsembe zachabechabe; nsembe zofukiza zindinyansa; tsiku lokhala mwezi ndi Sabata, kumema misonkhano, sindingalole mphulupulu ndi misonkhano.


amene akhala pakati pa manda, ndi kugona m'malo am'tseri; amene adya nyama ya nkhumba, ndi msuzi wa zinthu zonyansa uli m'mbale zao;


Wakupha ng'ombe alingana ndi wakupha munthu; iye wapereka nsembe ya mwanawankhosa alingana ndi wothyola khosi la galu; wothira nsembe yaufa akunga wothira mwazi wa nkhumba; wofukiza lubani akunga wodalitsa fano; inde iwo asankha njira zaozao, ndipo moyo wao ukondwerera m'zonyansa zao;


Poyamba ndibwezera mphulupulu yao ndi tchimo lao chowirikiza; chifukwa anaipitsa dziko langa ndi mitembo ya zodetsedwa zao, nadzaza cholowa changa ndi zonyansa zao.


Tsiku lomwelo mwaipha, ndi m'mawa mwake muidye; ngati katsalirako kanthu tsiku lachitatu, muzikatentha ndi moto.


koma aliyense akudyako adzasenza mphulupulu yake, popeza waipsa chopatulidwa cha Yehova; ndi munthuyu amsadze, kumchotsa kwa anthu a mtundu wake.


Ng'ombe kapena nkhosa yokula kapena yochepa chiwalo, ikhale nsembe yaufulu; koma pa chowinda siidzalandirika.


Ndipo musamazilandira izi ku dzanja la mlendo ndi kubwera nazo zikhale chakudya cha Mulungu wanu; popeza zili nako kuvunda kwao; zili ndi chilema; sizidzalandirikira inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa