Levitiko 19:7 - Buku Lopatulika7 Akakadya konse tsiku lachitatu kali chonyansa, kosavomerezeka: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Akakadya konse tsiku lachitatu kali chonyansa, kosavomerezeka: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Mukaidya pa tsiku lachitatu, kuteroko nkuchita chinthu chonyansa, ndipo nsembeyo sidzalandiridwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Ngati mudya choperekacho tsiku lachitatu, ndiye kuti mwachita chonyansa ndipo chakudyacho sichidzalandiridwa. Onani mutuwo |