Levitiko 19:4 - Buku Lopatulika4 Musamatembenukira mafano, kapena kudzipangira mulungu woyenga; Ine ndine Yehova Mulungu wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Musamatembenukira mafano, kapena kudzipangira mulungu woyenga; Ine ndine Yehova Mulungu wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Musabwerere ku mafano, kapena kudzipangira nokha milungu ya zitsulo zosungunula. Ine ndine Chauta, Mulungu wanu.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 “ ‘Musatembenukire ku mafano kapena kudzipangira nokha milungu ya zitsulo zosungunula. Ine ndine Yehova Mulungu wanu. Onani mutuwo |