Levitiko 19:2 - Buku Lopatulika2 Nena ndi khamu lonse la ana a Israele, nuti nao, Muzikhala oyera; pakuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu, ndine woyera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nena ndi khamu lonse la ana a Israele, nuti nao, Muzikhala oyera; pakuti Ine ndine Yehova Mulungu wanu, ndine woyera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Uza mpingo wonse wa Aisraele kuti, ‘Mukhale oyera pakuti Ine Chauta, Mulungu wanu, ndine woyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Uza gulu lonse la Aisraeli kuti, ‘Khalani oyera mtima chifukwa Ine, Yehova Mulungu wanu, ndine Woyera. Onani mutuwo |