Levitiko 19:12 - Buku Lopatulika12 Musamalumbira monama ndi kutchula dzina langa, ungaipse dzina la Mulungu wako; Ine ndine Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Musamalumbira monama ndi kutchula dzina langa, ungaipse dzina la Mulungu wako; Ine ndine Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Musalumbire m'dzina langa monyenga ndi kumaipitsa dzina la Ine Mulungu wanu pakutero. Ine ndine Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 “ ‘Musalumbire mʼdzina langa monyenga popeza kutero ndi kuyipitsa dzina la Mulungu wanu. Ine ndine Yehova. Onani mutuwo |