Levitiko 18:9 - Buku Lopatulika9 Usamavula mlongo wako, mwana wamkazi wa atate wako, kapena mwana wamkazi wa mai wako, wobadwa kwanu, kapena wobadwa kwina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Usamavula mlongo wako, mwana wamkazi wa atate wako, kapena mwana wamkazi wa mai wako, wobadwa kwanu, kapena wobadwa kwina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Usagone ndi mlongo wako, mwana wamkazi wa bambo wako, kapena mwana wamkazi wa mai wako, ngakhale abadwire kwanu kapena kuchilendo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “ ‘Usagonane ndi mlongo wako, mwana wamkazi wa abambo ako, kapena mwana wamkazi wa amayi ako, kaya anabadwira mʼnyumba mwanu kapena kwina. Onani mutuwo |