Levitiko 18:7 - Buku Lopatulika7 Usamavula atate wako, ndi mai wako; ndiye mai wako, usamamvula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Usamavula atate wako, ndi mai wako; ndiye mai wako, usamamvula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Usachititse manyazi bambo wako pakugona ndi mai wako. Ameneyo ndi mai wako, usamchititse manyazi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “ ‘Usachititse manyazi abambo ako pogonana ndi amayi ako. Iwo ndi amayi ako. Usagonane nawo. Onani mutuwo |