Levitiko 18:6 - Buku Lopatulika6 Asasendere mmodzi wa inu kwa mbale wake kumvula; Ine ndine Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Asasendere mmodzi wa inu kwa mbale wake kumvula; Ine ndine Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 “Munthu wina aliyense mwa inu asagone ndi wachibale wake. Ine ndine Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 “ ‘Munthu aliyense asagonane ndi wachibale wake. Ine ndine Yehova. Onani mutuwo |