Levitiko 18:5 - Buku Lopatulika5 Inde, muzisunga malemba anga, ndi maweruzo anga; amenewo munthu akawachita, adzakhala nao ndi moyo; Ine ndine Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Inde, muzisunga malemba anga, ndi maweruzo anga; amenewo munthu akawachita, adzakhala nao ndi moyo; Ine ndine Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Nchifukwa chake muchite zimene ndikukulamulani ndipo muzimvera malamulo anga, motero mudzakhala ndi moyo. Ine ndine Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Choncho sungani malangizo ndi malamulo anga, popeza munthu amene amvera zimenezi adzakhala ndi moyo. Ine ndine Yehova. Onani mutuwo |