Levitiko 18:4 - Buku Lopatulika4 Muzichita maweruzo anga, ndi kusunga malemba anga, kumayenda m'mwemo; Ine ndine Yehova Mulungu wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Muzichita maweruzo anga, ndi kusunga malemba anga, kumayenda m'mwemo; Ine ndine Yehova Mulungu wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Muzichita zimene ndikukulamulani, ndi kutsata malamulo anga ndi kuŵamvera. Ine ndine Chauta, Mulungu wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Inu muzimvera malamulo anga ndipo muzisamalitsa kutsatira malangizo anga. Ine ndine Yehova Mulungu wanu. Onani mutuwo |