Levitiko 18:18 - Buku Lopatulika18 Usamtenga mkazi kumuonjezera kwa mbale wake, kumvula, kumvula pamodzi ndi mnzake, akali ndi moyo mnzakeyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Usamtenga mkazi kumuonjezera kwa mbale wake, kumvuta, kumvula pamodzi ndi mnzake, akali ndi moyo mnzakeyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Ndipo usakwatire mbale wa mkazi wako ndi kumuvula pamene mbale wako ali moyo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 “ ‘Usakwatire mchemwali wa mkazi wako ndi kumagonana naye mkazi wakoyo ali moyo ngati wopikisana naye. Onani mutuwo |