Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 18:17 - Buku Lopatulika

17 Usamavula mkazi ndi mwana wamkazi wake; usamatenga mwana wamkazi wa mwana wamwamuna wake, kapena mwana wamkazi wa mwana wamkazi wake kumvula; ndiwo abale; chochititsa manyazi ichi.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Usamavula mkazi ndi mwana wamkazi wake; usamatenga mwana wamkazi wa mwana wamwamuna wake, kapena mwana wamkazi wa mwana wamkazi wake kumvula; ndiwo abale; chochititsa manyazi ichi.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Usagone ndi mkazi ndiponso ndi mwana wamkazi wa mkaziyo, ndipo usagone ndi mwana wamkazi wa mwana wake wamwamuna, kapena mwana wamkazi wa mwana wake wamkazi. Amenewo ndi thupi lake la mkaziyo, ndipo kuteroko nkuchita chinthu choipa kwambiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 “ ‘Usagonane ndi mkazi ndiponso mwana wake wamkazi. Usagonane ndi mwana wamkazi wa mwana wake wamwamuna, kapena mwana wamkazi wa mwana wake wamkazi. Amenewo ndi thupi limodzi ndi mkaziyo. Kutero ndikuchita chinthu choyipa kwambiri.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 18:17
4 Mawu Ofanana  

Usamtenga mkazi kumuonjezera kwa mbale wake, kumvula, kumvula pamodzi ndi mnzake, akali ndi moyo mnzakeyo.


Munthu akatenga mkazi pamodzi ndi mai wake chochititsa manyazi ichi; aziwatentha ndi moto, iye ndi iwowa; kuti pasakhale chochititsa manyazicho pakati pa inu.


ndiwo amene aliralira fumbi lapansi lili pamutu pa wosauka, napotoza njira ya wofatsa; ndipo munthu ndi atate wake amuka kwa namwali yemweyo, kuti aipse dzina langa loyera;


Wotembereredwa iye wakugona ndi mpongozi wake. Ndi anthu onse anene, Amen.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa