Levitiko 18:16 - Buku Lopatulika16 Usamavula mkazi wa mbale wako; ndiye thupi la mbale wako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Usamavula mkazi wa mbale wako; ndiye thupi la mbale wako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Usagone ndi mkazi wa mbale wako, chifukwa kuteroko nkuvula mbale wako. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 “ ‘Usagonane ndi mkazi wa mchimwene wako popeza potero ukuchititsa manyazi mʼbale wakoyo. Onani mutuwo |