Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 18:14 - Buku Lopatulika

14 Usamavula mbale wa atate wako; usamasendera kwa mkazi wake; ndiye mai wako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Usamavula mbale wa atate wako; usamasendera kwa mkazi wake; ndiye mai wako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Usagone ndi mkazi wa mbale wa bambo wako, poti ameneyo ndi mai wako.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 “ ‘Usachititse manyazi mchimwene wa abambo ako pogonana ndi mkazi wake popeza amenewo ndi azakhali ako.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 18:14
2 Mawu Ofanana  

Usamavula mbale wa mai wako; popeza ndiye mbale wa mai wako.


Munthu akagona ndi mkazi wa mbale wa atate wake, navula mbale wa atate wake; asenze kuchimwa kwao; adzafa osaona ana.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa