Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Levitiko 18:13 - Buku Lopatulika

13 Usamavula mbale wa mai wako; popeza ndiye mbale wa mai wako.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Usamavula mbale wa mai wako; popeza ndiye mbale wa mai wako.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Usagone ndi mbale wa mai wako, poti ameneyo ndi thupi limodzi ndi mai wako.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 “ ‘Usagonane ndi mchemwali wa amayi ako chifukwa ameneyo ndi thupi limodzi ndi amayi ako.

Onani mutuwo Koperani




Levitiko 18:13
3 Mawu Ofanana  

Usamavula mlongo wa atate wako; ndiye wa chibale cha atate wako.


Usamavula mbale wa atate wako; usamasendera kwa mkazi wake; ndiye mai wako.


Usamavula mbale wa mai wako, kapena mlongo wa atate wako; popeza anavula abale ake; asenze mphulupulu yao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa